1 line
279 B
Plaintext
1 line
279 B
Plaintext
\v 8 Koma Rehobowamu ananyalanyaza uphungu wa akuluwo adamlangiza, nafunsira kwa anyamata anakulira naye, akuima pamaso pake. \v 9 Ndipo iye anati kwa iwo, Mundipangiranji uphungu, kuti tiyankhe anthu amene analankhula nane, kuti, Muchepetse goli limene atate wanu anatisenzetsa? |