nya-x-nyanja_2ch_text_reg/10/03.txt

1 line
460 B
Plaintext

\v 3 Mwamene umo banatumiza mau na kumuitana, ndipo Yelobowamu pamozi na Aislayeli bonse banabwela; bana kamba kwa Rehobowamu kuti, \v 4 "Ba tate bako banapangitsa goli yathu kunkala yovutisana. Chifukwa chakwe, panga ntchito ya ba tate bako kuti inkale yosavuta, futi upepukise goli yolema yamene banativalika, ndipo tizakutumikilani." \v 5 Rehobowamu anaba yanka kuti, "Mubwele futi kuli ine pakapita masiku yatatu." Mwamene umo bantu bananyamuka naku yenda.