nya-x-nyanja_2ch_text_reg/09/27.txt

1 line
234 B
Plaintext

\v 27 Mfumu inali na siliva mu Yerusalemu, monga chabe minyala ili pansi. Anapanganso matabwa a mukunguza yolingana na mitengo ya mukuyu yamene ili ku chigwa. \v 28 Banabwelesa mahachi ya Solomoni kuchokela ku Igupto na maziko yonse.