nya-x-nyanja_2ch_text_reg/09/25.txt

1 line
244 B
Plaintext

\v 25 Solomoni anali na makola 4,000 ya mahachi na magaleta, na bapakavalo 12,000, bamene anayika mumizinda ya magaleta na ku Yerusalemu. \v 26 Anakalamulila mafumu yonse kuyambila ku Mumana mpaka ku ziko ya Afilisiti, mpaka kumalile na Igupto.