nya-x-nyanja_2ch_text_reg/07/21.txt

1 line
436 B
Plaintext

\v 21 Ngakhale iyi tempele niyokwela kwambili, aliyense wamene azapita pafupi azadabwa eka. Bazafunsa kuti, 'Nichifukwa chani Yehova achita izi ziko lino na nyumba iyi?' \v 22 Benangu bazayanka, 'Chifukwa banakana Yehova, Mulungu wawo, wamene anabwelesa makolo yawo kuchoka mu ziko ya Aiguputo, ndipo banagwililila milungu inangu ndi kuigwadira na kuigwadia na kuipembeza. Ndiye chifukwa chake Yehova abwelesa chionongeko ichi chonse."