nya-x-nyanja_2ch_text_reg/07/16.txt

1 line
477 B
Plaintext

\v 16 Chifukwa nasanka na kupatula ino nyumba kuti zina yanga izankalapo muyayaya. Menso yanga na mutima wanga yazankala kwamene uko masiku yonse. \v 17 Koma iwe, ukayenda pamenso panga monga Davide batate bako banayendela, kumvelela vonse vamene nakulamulila, na kusunga malamulo yanga, malemba anga, \v 18 nizankazikisa mupando wako wachifumu, monga ninakambila muchipangano na Davide batate bako , pamene ninakamba kuti, 'Mwana wako sazakangiwa kunkala olamulila Isiraeli.'