nya-x-nyanja_2ch_text_reg/07/08.txt

1 line
549 B
Plaintext

\v 8 Ndipo Solomoni anachita chikondwelelo masiku yali 7, na bonse ba Israeli, musonkano waukulu kwambili, kuchokela ku Lebo Hamati mpaka ku mumana wa ku Igupto. \v 9 Pa siku lachisanu na chitatu anachita musonkano waukulu, chifukwa anapatulila guwa ya bansembe masiku yasanu na yabili, na madyelelo masiku yasanu na yabili. \v 10 Pa siku ya 23 ya mwezi wachisanu na chibili, Solomoni anatuma bantu kuti bayende ku matenti yawo na chimwemwe na mitima yokondwela chifukwa cha zabwino zamene Yehova anachitila Davide, Solomoni, na Israeli, bantu bake.