Thu Apr 18 2024 11:54:18 GMT+0200 (South Africa Standard Time)
This commit is contained in:
parent
ed5947e5cc
commit
c47e6b0697
|
@ -1 +1 @@
|
|||
\v 10 \v 11 Choncho anasonkhana ku Yerusalemu m’mwezi wachitatu, m’chaka cha 15 cha ulamuliro wa Asa. Anaphera Yehova nsembe tsiku limenelo zina mwa zofunkha zimene anabwera nazo, ng’ombe mazana asanu ndi awiri, ndi nkhosa ndi mbuzi zikwi zisanu ndi ziwiri.
|
||||
\v 10 Choncho anasonkhana ku Yerusalemu m’mwezi wachitatu, m’chaka cha 15 cha ulamuliro wa Asa. \v 11 Anaphera Yehova nsembe tsiku limenelo zina mwa zofunkha zimene anabwera nazo, ng’ombe mazana asanu ndi awiri, ndi nkhosa ndi mbuzi zikwi zisanu ndi ziwiri.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 12 Iwo anachita pangano kuti afunefune Yehova Mulungu wa makolo awo ndi mtima wawo wonse ndi moyo wawo wonse. \v 13 Iwo anagwirizana kuti aliyense amene akana kufunafuna Yehova Mulungu wa Isiraeli ayenera kuphedwa, kaya akhale wamng’ono kapena wamkulu, kaya akhale mwamuna kapena mkazi.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 14 \v 15 Iwo analumbira kwa Yehova ndi mawu aakulu, ndi kufuula, ndi malipenga ndi malipenga. Ayuda onse anakondwera ndi lumbirolo, pakuti analumbira ndi mtima wawo wonse, ndipo anafunafuna Mulungu ndi chikhumbo chawo chonse, ndipo anampeza. Yehova anawapatsa mtendere wowazungulira.
|
|
@ -167,8 +167,8 @@
|
|||
"15-03",
|
||||
"15-06",
|
||||
"15-08",
|
||||
"15-10",
|
||||
"15-12",
|
||||
"15-14",
|
||||
"15-16",
|
||||
"15-18",
|
||||
"16-title",
|
||||
|
|
Loading…
Reference in New Issue