Thu Apr 18 2024 11:10:11 GMT+0200 (South Africa Standard Time)
This commit is contained in:
parent
c4d5a62eb7
commit
7263a224ac
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 2 Koma mawu a Yehova anadza kwa Semaya munthu wa Mulungu woona, kuti: \v 3 “Uza Rehobowamu mwana wa Solomo mfumu ya Yuda ndi Aisiraeli onse a ku Yuda ndi Benjamini kuti, \v 4 ‘Yehova wanena kuti, ‘Musamamenye nkhondo kapena kuchita nkhondo. abale anu. Aliyense abwerere kunyumba kwake, chifukwa ineyo ndachititsa zimenezi.”’” Choncho iwo anamvera mawu a Yehova ndipo anasiya kumenyana ndi Yerobowamu.
|
Loading…
Reference in New Issue