Thu Apr 18 2024 11:24:16 GMT+0200 (South Africa Standard Time)
This commit is contained in:
parent
746e40faec
commit
5f42c518d7
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 2 M’chaka chachisanu cha Mfumu Rehobowamu, + Sisaki mfumu ya Iguputo inabwera kudzamenyana ndi Yerusalemu chifukwa anthuwo sanalakwire Yehova. \v 3 Anadza ndi magareta mazana khumi ndi awiri, ndi apakavalo zikwi makumi asanu ndi limodzi. Ankhondo osawerengeka anadza naye ku Igupto: Alibiya, Suki, ndi Akusi. \v 4 Analanda mizinda yokhala ndi mipanda yolimba kwambiri ya Yuda n’kupita ku Yerusalemu.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 5 Tsopano mneneri Semaya anabwera kwa Rehobowamu ndi kwa atsogoleri a Yuda amene anasonkhana ku Yerusalemu chifukwa cha Sisaki. Semaya anati kwa iwo, Atero Yehova, Inu mwandisiya ine, chotero inenso ndakuperekani m’dzanja la Sisaki. \v 6 Pamenepo akalonga a Israyeli ndi mfumu anadzichepetsa, nati, Yehova ndiye wolungama.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
Yehova ataona kuti adzicepetsa, mau a Yehova anadza kwa Semaya, kuti, Adzicepetsa, sindidzawaononga; Ngakhale zili choncho, adzakhala atumiki ake, kuti amvetse tanthauzo la kunditumikira + ndi kutumikira olamulira a mayiko ena.”
|
|
@ -140,7 +140,6 @@
|
|||
"12-01",
|
||||
"12-02",
|
||||
"12-05",
|
||||
"12-07",
|
||||
"12-09",
|
||||
"12-11",
|
||||
"12-13",
|
||||
|
|
Loading…
Reference in New Issue