Thu Apr 18 2024 11:16:13 GMT+0200 (South Africa Standard Time)
This commit is contained in:
parent
65170d9384
commit
2d4db9c00b
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 13 Ansembe ndi Alevi amene anali mu Isiraeli yense anapita kwa iye kuchokera m’malire awo. \v 14 Pakuti Alevi anasiya malo awo odyetserako ziweto ndi chuma chawo kuti abwere ku Yuda ndi ku Yerusalemu, pakuti Yerobiamu ndi ana ake anawathamangitsa, moti sanathenso kukhala ansembe a Yehova. \v 15 Yerobiamu anadzipangira ansembe a malo okwezeka, ndi mbuzi ndi ana a ng'ombe amene anapanga.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 16 Anthu a m’mafuko onse a Isiraeli anatsatira pambuyo pawo, amene anali kufunitsitsa kufunafuna Yehova Mulungu wa Isiraeli. anafika ku Yerusalemu kudzapereka nsembe kwa Yehova Mulungu wa makolo awo. \v 17 Chotero analimbitsa ufumu wa Yuda ndi kulimbitsa Rehobowamu mwana wa Solomo m’zaka zitatu, ndipo anayenda m’njira ya Davide ndi Solomo zaka zitatu.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 18 \v 19 Rehobowamu anadzitengera mkazi: Mahalati, mwana wamkazi wa Yerimoti, mwana wa Davide, ndi Abihaili, mwana wamkazi wa Eliyabu, mwana wa Jese. Iye anamuberekera ana aamuna: Yeusi, Semariya ndi Zahamu.
|
|
@ -133,7 +133,6 @@
|
|||
"11-11",
|
||||
"11-13",
|
||||
"11-16",
|
||||
"11-18",
|
||||
"11-20",
|
||||
"11-22",
|
||||
"12-title",
|
||||
|
|
Loading…
Reference in New Issue