Thu Apr 18 2024 11:36:17 GMT+0200 (South Africa Standard Time)

This commit is contained in:
Timothy Muzgatama 2024-04-18 11:36:18 +02:00
parent 60ae094980
commit 2234b8b7ed
4 changed files with 3 additions and 1 deletions

1
13/06.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\v 6 Koma Yerobiamu mwana wa Nebati, mtumiki wa Solomo mwana wa Davide, anaukira mbuye wake. \v 7 Anthu opanda pake, anthu opanda pake, anasonkhana kwa iye. Iwo anabwera kudzamenyana ndi Rehobowamu mwana wa Solomo, Rehobowamu ali wamngono ndi wantha mtima, + moti anamugonjetsa.

1
13/08.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\v 8 Chotero mukuganizira zolimbana ndi ufumu wa Yehova umene uli mmanja mwa ana a Davide, chifukwa ndinu gulu lankhondo lalikulu, ndipo muli ndi ana a ngombe agolide amene Yerobiamu anawapanga kuti akhale milungu yanu. \v 9 Koma simunapitikitsa ansembe a Yehova, zidzukulu za Aroni, ndi Alevi, ndi kudzipangira ansembe inu, monga amachitira anthu a mmaiko ena? Aliyense amene wabwera kudzatumikira monga wansembe ndi kupereka nsembe ngombe yaingono yamphongo ndi nkhosa zamphongo 7, adzakhala wansembe wa imene si milungu.

1
13/10.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
Koma ife, Yehova ndiye Mulungu wathu, + ndipo sitinamusiye. Tili ndi ansembe, zidzukulu za Aroni, otumikira Yehova, ndi Alevi amene amagwira ntchito yawo. Mmawa ndi madzulo onse amafukizira Yehova nsembe zopsereza ndi zofukiza zonunkhira bwino. + Iwo amakonzanso mkate woonekera patebulo loyera. azisamaliranso choikapo nyale chagolide, ndi nyali zake, aziyaka madzulo onse. Timasunga malamulo a Yehova Mulungu wathu, koma inu mwamusiya.

View File

@ -150,7 +150,6 @@
"13-04",
"13-06",
"13-08",
"13-10",
"13-12",
"13-13",
"13-16",