Thu Apr 18 2024 11:36:17 GMT+0200 (South Africa Standard Time)
This commit is contained in:
parent
60ae094980
commit
2234b8b7ed
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 6 Koma Yerobiamu mwana wa Nebati, mtumiki wa Solomo mwana wa Davide, anaukira mbuye wake. \v 7 Anthu opanda pake, anthu opanda pake, anasonkhana kwa iye. Iwo anabwera kudzamenyana ndi Rehobowamu mwana wa Solomo, Rehobowamu ali wamng’ono ndi wantha mtima, + moti anamugonjetsa.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 8 Chotero mukuganizira zolimbana ndi ufumu wa Yehova umene uli m’manja mwa ana a Davide, chifukwa ndinu gulu lankhondo lalikulu, ndipo muli ndi ana a ng’ombe agolide amene Yerobiamu anawapanga kuti akhale milungu yanu. \v 9 Koma simunapitikitsa ansembe a Yehova, zidzukulu za Aroni, ndi Alevi, ndi kudzipangira ansembe inu, monga amachitira anthu a m’maiko ena? Aliyense amene wabwera kudzatumikira monga wansembe ndi kupereka nsembe ng’ombe yaing’ono yamphongo ndi nkhosa zamphongo 7, adzakhala wansembe wa imene si milungu.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
Koma ife, Yehova ndiye Mulungu wathu, + ndipo sitinamusiye. Tili ndi ansembe, zidzukulu za Aroni, otumikira Yehova, ndi Alevi amene amagwira ntchito yawo. M’mawa ndi madzulo onse amafukizira Yehova nsembe zopsereza ndi zofukiza zonunkhira bwino. + Iwo amakonzanso mkate woonekera patebulo loyera. azisamaliranso choikapo nyale chagolide, ndi nyali zake, aziyaka madzulo onse. Timasunga malamulo a Yehova Mulungu wathu, koma inu mwamusiya.
|
|
@ -150,7 +150,6 @@
|
|||
"13-04",
|
||||
"13-06",
|
||||
"13-08",
|
||||
"13-10",
|
||||
"13-12",
|
||||
"13-13",
|
||||
"13-16",
|
||||
|
|
Loading…
Reference in New Issue