1 line
413 B
Plaintext
1 line
413 B
Plaintext
\v 29 Nkhani zina zokhudza Rehobowamu ndi zonse zimene anachita, zinalembedwa m’buku la zochitika za m’masiku a mafumu a Yuda. \v 30 Panali nkhondo yokhazikika pakati pa Rehobowamu ndi Yerobiamu. \v 31 Choncho Rehobowamu anagona pamodzi ndi makolo ake ndipo anaikidwa m’manda pamodzi ndi makolo ake mu Mzinda wa Davide. Dzina la amayi ake linali Naama Mamoni. Abiya mwana wake anakhala mfumu m’malo mwake. |