1 line
417 B
Plaintext
1 line
417 B
Plaintext
\v 9 M’malo mwake, wachita zoipa kwambiri kuposa onse amene anakhalapo iwe usanakhale. Wapanga milungu yina, ndi kupanga mafano osungunula kuti undikwiyitse, ndipo unandikankha kumbuyo kwako. \v 10 Cifukwa cace taonani, ndidzatengera nyumba ya Yerobiamu coipa; Ndidzapha ana onse aamuna mu Isiraeli, kaya akhale kapolo kapena mfulu, ndipo ndidzachotsa nyumba ya Yerobiamu ngati munthu wotenthetsa ndowe mpaka kutha. |