nya-x-nyanja_1ki_text_reg/20/22.txt

1 line
425 B
Plaintext

\v 22 Manje muneneli anabwela kuli mfumu ya Isilayeli nakukamba kuli yeve," Yenda, ukazilimbise, na kumvesesa na kukonza vameme uchita, chifukwa pakusila kwa chaka mfumu ya Aramu izabwela kumenyana naiwe futi. \v 23 Banchito ba mfumu ya Aramu banakamba kuli eve, "Mulungu wabo ni Mulungu wa mapili. Ndiye chifukwa chake benze nampamvu kuchila ise. Koma manje tiyeni timenyane nabo muchigwa, ndipo tizankala bolimba kubachila.