|
\v 62 Mwaichi mfumu na bonse Israeli bonse pamozi naye anapeleka nsembe kwa Yehova. \v 63 Solomo anapereka nsembe yoyamika kwa Yehova: ng'ombe zikwi makumi awili mphambu zibilii, na nkhosa 120,000. Momwemo mfumu na bana bonse ba Israyeli banapatula nyumba ya Yehova. |