1 line
337 B
Plaintext
1 line
337 B
Plaintext
\v 33 Pamene banthu bako ba Israeli bagonjesedwa kuli badani chifukwa bakuchimwilani imwe, ngati batenukila kuli imwe, kukambilila pa zina yanu, nakupempela, nakufuna ubwino wanu mu tempele ino- \v 34 napapata nvelani kuchoka mumwamba na kukulukilila uchimo wa banthu banu ba Israeli; babweleseni futi kumalo yamene munapasa makolo yawo. |