nya-x-nyanja_1ki_text_reg/08/37.txt

1 line
439 B
Plaintext

\v 37 Tiyerekeze kuti m'dziko mwanu muli njala, kapena ngati muli matenda, chimphepo kapena kachilombo, dzombe kapena malasankhuli; kapena kuti ngati mdani aukira zipata za mudzi m'dziko lao, kapena kuti pali mliri uli wonse kapena matenda; \v 38 ndipo bwanji ngati mapemphero ndi zopempha zichokera kwa munthu, kapena ndi anthu anu onse a Israyeli, ali yense akudziwa mliriwo mumtima mwake; akutambasulira manja ake kuloza ku Kachisi uyu.