nya-x-nyanja_1ki_text_reg/08/09.txt

1 line
363 B
Plaintext

\v 9 Munalibe kanthu m'likasamo kupatula miyala iwiriyo anaiyika Mose ku Horebe, pamene Yehova anachita pangano ndi ana a Israyeli, atatuluka m'dziko la Aigupto. \v 10 Ndipo panali, pamene ansembe anatuluka m'malo opatulika, mtambo unadzaza kachisi wa Yehova. \v 11 Ansembe sanathe kuimirira chifukwa cha mtambowo, pakuti ulemerero wa Yehova unadzaza nyumba yake.