1 line
307 B
Plaintext
1 line
307 B
Plaintext
\v 45 Nkhani zina zokhudza Yehosafati ndi mphamvu zimene anachita, ndi mmene anamenyera nkhondo, zinalembedwa m’buku la zochitika za mafumu a Yuda. \v 46 Anachotsa m’dziko mahule ena onse amene anatsala m’masiku a bambo ake Asa. \v 47 Munalibe mfumu ku Edomu koma wachiwiri wake ankalamulira kumeneko. |