This file contains Unicode characters that might be confused with other characters. If you think that this is intentional, you can safely ignore this warning. Use the Escape button to reveal them.
\v 43 Iye anayenda m’njira za atate wake Asa; sanapatuke kwa iwo; Iye anachita zoyenera pamaso pa Yehova. Koma misanje sinachotsedwe. Anthu anali kuperekabe nsembe ndi kufukiza pamisanje. \v 44 Yehosafati anachita mtendere ndi mfumu ya Isiraeli.