1 line
295 B
Plaintext
1 line
295 B
Plaintext
\v 41 Kenako Yehosafati mwana wa Asa anayamba kulamulira Yuda m’chaka chachinayi cha Ahabu mfumu ya Isiraeli. \v 42 Yehosafati anali wa zaka makumi atatu kudza zisanu polowa ufumu wace, nakhala mfumu m'Yerusalemu zaka makumi awiri mphambu zisanu. Dzina la amayi ake linali Azuba mwana wa Sili. |