1 line
311 B
Plaintext
1 line
311 B
Plaintext
\v 39 Nkhani zina zokhudza Ahabu ndi zonse zimene anachita, nyumba ya minyanga ya njovu imene anamanga ndi mizinda yonse imene anamanga, zinalembedwa m’buku la zochitika za mafumu a Isiraeli kodi? \v 40 Choncho Ahabu anagona pamodzi ndi makolo ake, ndipo Ahaziya mwana wake anayamba kulamulira m’malo mwake. |