1 line
300 B
Plaintext
1 line
300 B
Plaintext
\v 35 Nkhondoyo inakula tsiku lomwelo, ndipo mfumu inaimitsidwa m’galeta lake pamaso pa Aaramu. Iye anafa madzulo. Mwazi unatuluka m’balalo n’kulowa pansi pa gareta. \v 36 Pamenepo dzuwa linali kulowa, anthu anafuula kuti: “Aliyense abwerere kumudzi wake, ndipo aliyense abwerere kudera lake. |