nya-x-nyanja_1ki_text_reg/22/34.txt

1 line
224 B
Plaintext

\v 34 Koma munthu wina anaponya uta wake mwachisawawa, nalasa mfumu ya Israyeli pakati pa mfundo za zida zake. Pamenepo Ahabu anauza woyendetsa galeta lake kuti: “Tembenuka unditulutse kunkhondo, pakuti ndavulala kwambiri.