1 line
493 B
Plaintext
1 line
493 B
Plaintext
\v 10 Ndipo Ahabu mfumu ya Israyeli ndi Yehosafati mfumu ya Yuda anakhala yense pa mpando wacifumu, atabvala zobvala zao, pa dwale pa cipata ca Samariya; ndipo aneneri onse anali kunenera pamaso pao. \v 11 Zedekiya mwana wa Kenaana anadzipangira nyanga zachitsulo n’kunena kuti: “Yehova wanena kuti, ‘Ndi nyangazi mudzakantha Aaramu mpaka kuwatha.’” \v 12 Aneneri onsewo analosera mofananamo kuti: “Kanthani Ramoti Giliyadi ndipo mudzapambana. Yehova waupereka m’manja mwa mfumu. |