1 line
496 B
Plaintext
1 line
496 B
Plaintext
\v 7 Koma Yehosafati anati, Kodi pano palibenso mneneri wina wa Yehova amene tingapemphe malangizo kwa iye? \v 8 Mfumu ya Isiraeli inauza Yehosafati kuti: “Pali munthu mmodzi amene tingapemphe malangizo kwa Yehova kuti atithandize, ndiye Mikaya mwana wa Imla, koma ndimadana naye chifukwa salosera zabwino za ine, koma zowawa. Koma Yehosafati anati, Mfumu isatero. \v 9 Kenako mfumu ya Isiraeli inaitana kapitawo wa asilikali n’kumuuza kuti: “Bwera naye Mikaya mwana wa Imla nthawi yomweyo. |