1 line
291 B
Plaintext
1 line
291 B
Plaintext
\v 21 Yehova atero kwa iwe, Taona, ndidzakutengera tsoka, ndi kutha ndi kupha Ahabu ana aamuna onse, ndi kapolo, ndi mfulu m’Israyeli; \v 22 Ndidzayesa banja lako ngati banja la Yerobiamu mwana wa Nebati, ndi banja la Basa mwana wa Ahiya, popeza wandikwiyitsa ine, ndi kucimwitsa Israyeli. |