1 line
358 B
Plaintext
1 line
358 B
Plaintext
\v 19 Ukamuuze kuti Yehova akuti, 'Kodi wapha ndi kulanda? Pamenepo udzamuuza kuti Yehova akuti, ‘Pamalo pamene agalu ananyambita magazi a Naboti, agalu adzanyambita magazi ako, inde magazi ako.’” \v 20 Ahabu anauza Eliya kuti: “Kodi wandipeza mdani wanga? Eliya anayankha kuti: “Ndakupeza, chifukwa wadzigulitsa kuti uchite zoipa pamaso pa Yehova. |