This file contains Unicode characters that might be confused with other characters. If you think that this is intentional, you can safely ignore this warning. Use the Escape button to reveal them.
\v 4 Mkazi wa Yerobiamu anachita chomwecho; Kenako ananyamuka n’kupita ku Silo n’kukafika kunyumba ya Ahiya. Koma Ahiya sanatha kuona; anasiya kuona chifukwa cha ukalamba. \v 5 Yehova anati kwa Ahiya, Taona, mkazi wa Yerobiamu akudza kudzafunsira kwa iwe za mwana wake; ."