nya-x-nyanja_1ki_text_reg/13/11.txt

1 line
507 B
Plaintext

\v 11 Manje panali mneneli mukulu wamene ankakala ku Beteli, ndipo umozi mwana wake paba muna anabwela kumu uza vonse vamene kapolo wa Mulungu anachita pa siku ija mu Beteli. bana bake bamuna banamu uza mau yamene kapolo wa Mulungu anakamba kuli mfumu. \v 12 Ba tate babo banakamba kuli beve, "Anayenda njila iti?" Manje bana bake ba muna banaona njila ya kapolo wa Mulungu yochokela ku Yuda. \v 13 Ndipo anakamba kuli bana bake bamuna, Nimangileni mbela pa bulu wake. Ndipo anamangilila bulu, naku; ikwela.