nya-x-nyanja_1ki_text_reg/13/04.txt

1 line
422 B
Plaintext

\v 4 Pamene mfumu ananvela vamene mwana mwamuna wa Mulungu anakamba, kuti analilila guwa yansembe ku Beteli, Yeroboamu anatambulula kwanja yake kuchokela pa guwa, kukamba, “Mgwileni.” kwanja yamene anatambulula mwamuna inayuma, kuti asabwewlele kuli eve. \v 5 (Guwa yansembe inagabanikana ndipo milota inasanulidwa paguwa, monga kunalongosolela na chilangizo chamene munthu wa Mulungu uja anapleleka mu mau ya Yahweh.)