nya-x-nyanja_1ki_text_reg/11/11.txt

1 line
461 B
Plaintext
Raw Permalink Blame History

This file contains ambiguous Unicode characters

This file contains Unicode characters that might be confused with other characters. If you think that this is intentional, you can safely ignore this warning. Use the Escape button to reveal them.

\v 11 Choncho Yehova anauza Solomo kuti: “Popeza wachita zimenezi, osasunga pangano ndi malemba anga amene ndinakulamulira, ndithu ndidzangamba ufumuwo kuuchotsa kwa iwe ndi kuupereka kwa mtumiki wako, \v 12 koma chifukwa cha Davide atate wako. Sindidzachita zimenezi udakali ndi moyo, koma ndidzaukhadzula mmanja mwa mwana wako, \v 13 koma ndidzaupereka kwa mwana wako fuko limodzi chifukwa cha Davide mtumiki wanga wa Yerusalemu, umene ndausankha.”