1 line
293 B
Plaintext
1 line
293 B
Plaintext
\v 26 Solomoni anasonkhanitsa magaleta ndi apakavalo. Anali ndi magareta 1,400 ndi apakavalo 12,000 amene anawaika m’mizinda ya magaleta ndiponso ku Yerusalemu. \v 27 Mfumuyo inali ndi siliva ku Yerusalemu ngati miyala yapansi. Anachulukitsa mitengo ya mkungudza + ngati mikuyu ya m’zigwa. |