1 line
351 B
Plaintext
1 line
351 B
Plaintext
\v 16 Mfumu Solomo inapanga zishango zazikulu mazana awiri zagolide wosakaniza ndi zitsulo zina. Masekeli mazana asanu ndi limodzi a golidi analowa m'modzi. \v 17 Anapanganso zishango mazana atatu zagolide wosakaniza ndi zitsulo zina. chishango chilichonse chinali ndi mamina atatu agolidi; mfumu inawaika m’nyumba ya mfumu ya Nkhalango ya Lebanoni. |