nya-x-nyanja_1ki_text_reg/08/33.txt

1 line
337 B
Plaintext

\v 33 Pamene banthu bako ba Israeli bagonjesedwa kuli badani chifukwa bakuchimwilani imwe, ngati batenukila kuli imwe, kukambilila pa zina yanu, nakupempela, nakufuna ubwino wanu mu tempele ino- \v 34 napapata nvelani kuchoka mumwamba na kukulukilila uchimo wa banthu banu ba Israeli; babweleseni futi kumalo yamene munapasa makolo yawo.