nya-x-nyanja_1ki_text_reg/08/20.txt

1 line
365 B
Plaintext

\v 20 Yehova wakwanilisa mawu yamene anakamba, chifukwa nanyamuka mumalo mwa Davide batate banga, ndipo ninkala pamupando wachifumu wa Israyeli, monga Yehova anakamba. \v 21 Namanga nyumba mu zina ya Yehova, Mulungu wa Israyeli. Napanga malo ya likasa kwamene kuja, mwamene muli chipangano cha Yehova, chamene anapangana na makolo bathu pobachosa muziko ya Aigupto.