nya-x-nyanja_1ki_text_reg/08/06.txt

1 line
462 B
Plaintext

\v 6 Bansembe banangenesa likasa la chipangano cha Yehova kumalo yake, ku chipinda chamukati cha munyumba, Malo yoyela yopambana, pansi pa mapipiko ya Akerubi. \v 7 Chifukwa Akerubi banatambasula mapipiko yawo kumalo kwa Likasa, na kuvininkila Likasa na mitengo yake yonyamulila. \v 8 Mitengo inali itali kwambili chakuti kosilizila kwake yanali kuonekela kuchokela kumalo yoyela kusogolo kwa chipinda chamukati, koma siyanali kuonekela panja. yalipo mpaka lelo.