nya-x-nyanja_1ki_text_reg/01/43.txt

1 line
464 B
Plaintext

\v 43 Pameneapo Jonathani anayankha Adoniya kuti, “Bwana wathu Mfumu Davide wayika Solomoni kunkhala mfumu, \v 44 ndipo atumiza wansembe Zadoki, Nathani muneneli, Benaya mwana wa Yehoyada, ma Kerethitesi na Pelethitesi. Bana yenza Solomoni pa bulu yama mfumu Davide. \v 45 Zadoki wansembe na Nathani mneneli anamuzoza kuti ankhale mfumu ku Gihoni, ndipo abwela kwameneuko alikusangalala, pakuti mu muzinda wonse wasanduka phokoso. Ndiye phokoso yamene mwamvela.