nya-x-nyanja_1ki_text_reg/01/09.txt

1 line
308 B
Plaintext

\v 9 Adoniya anapeleka nsembe ya nkosa, na ngombe, ngombe yamafuta pafupi na mwala wa Zoheleti, pafupi na Eni Rogeli. Anaitana abale bake bonse, bana bamuna ba mfumu, na bamuna bonse ba ku Yuda, banchito ba mfumu. \v 10 Koma sanayitane Nathani muneneli, Benaya, bamuna bampamvu, kapena Solomoni mubale wake.