Thu Oct 07 2021 20:23:41 GMT+0200 (Central Africa Time)
This commit is contained in:
parent
e17a3fd768
commit
f2c3983d14
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 59 Lolani mawu awa ndalankhula, amene ndapempha pamaso pa Yehova, akhale pafupi ndi Yehova Mulungu wathu usana ndi usiku, kuti athandize pa ntchito ya mtumiki wake ndi mlandu wa anthu ake Israyeli, monga zifunikira tsiku ndi tsiku; \v 60 kuti anthu onse a dziko lapansi adziwe kuti Yehova ndiye Mulungu, ndipo palibenso Mulungu wina; \v 61 Potero mtima wanu ukhale wokhulupirika kwa Yehova Mulungu wathu, kuyenda m'malemba ace, ndi kusunga malamulo ake, monga lero. "
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 62 Kotero mfumu ndi Aisraeli onse pamodzi naye anapereka nsembe kwa Yehova. \v 63 Solomo anapereka nsembe yoyamika kwa Yehova: ng'ombe zikwi makumi awiri mphambu ziwiri, ndi nkhosa 120,000. Momwemo mfumu ndi ana onse a Israyeli anapatula nyumba ya Yehova.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 64 Tsiku lomwelo mfumu inapatula pakati pa bwalo patsogolo pa kacisi wa Yehova; pakuti pamenepo anapereka nsembe zopsereza, ndi nsembe zambewu, ndi mafuta a nsembe zoyamika; zing'onozing'ono kulandira nsembe yopsereza, nsembe yambewu, ndi mafuta a nsembe zoyamika.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 65 Pamenepo Solomo anacita madyerero nthawi yomweyo, ndi Aisrayeli onse naye, msonkhano waukulu, kuyambira ku Lebano Hamati kufikira ku mtsinje wa Aigupto, pamaso pa Yehova Mulungu wathu masiku asanu ndi awiri, enanso masiku asanu ndi awiri, ndiwo masiku khumi ndi anayi. \v 66 Pa tsiku lachisanu ndi chitatu anawalola anthu kuti apite, ndipo iwo anadalitsa mfumuyo ndi kupita kwawo ndi chimwemwe ndi mtima wokondwa chifukwa cha zabwino zonse zimene Yehova anachitira Davide mtumiki wake, ndi Israeli, anthu ake.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
Mutu 9
|
|
@ -186,6 +186,11 @@
|
|||
"08-49",
|
||||
"08-51",
|
||||
"08-54",
|
||||
"08-57"
|
||||
"08-57",
|
||||
"08-59",
|
||||
"08-62",
|
||||
"08-64",
|
||||
"08-65",
|
||||
"09-title"
|
||||
]
|
||||
}
|
Loading…
Reference in New Issue