Thu Apr 18 2024 16:02:39 GMT+0200 (South Africa Standard Time)
This commit is contained in:
parent
2abe9da812
commit
ec303e41fa
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 19 Nkhani zina zokhudza Yerobiamu, mmene anamenyera nkhondo+ ndi mmene analamulirira, zinalembedwa m’buku la zochitika za mafumu a Isiraeli. \v 20 Yerobiamu analamulira zaka 22, ndipo anagona pamodzi ndi makolo ake, ndipo Nadabu mwana wake anayamba kulamulira m’malo mwake.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 21 Tsopano Rehobowamu mwana wa Solomo anali kulamulira ku Yuda. Rehobowamu anali wa zaka 41 pamene anayamba kulamulira, ndipo analamulira zaka 17 ku Yerusalemu, mzinda umene Yehova anausankha mwa mafuko onse a Isiraeli kuti aikemo dzina lake. Dzina la amayi ake linali Naama Mamoni. \v 22 Yuda anacita coipa pamaso pa Yehova; anamcititsa nsanje ndi zocimwa zao, zopambana zonse anazicita makolo ao.
|
|
@ -283,7 +283,6 @@
|
|||
"14-14",
|
||||
"14-17",
|
||||
"14-19",
|
||||
"14-21",
|
||||
"14-23",
|
||||
"14-25",
|
||||
"14-27",
|
||||
|
|
Loading…
Reference in New Issue