Mon Jan 17 2022 15:09:09 GMT+0000 (Greenwich Mean Time)

This commit is contained in:
Timothy Muzgatama 2022-01-17 15:09:10 +00:00
commit cc07e49921
73 changed files with 76 additions and 85 deletions

1
01/01.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\c 1 \v 1 Mfumu Davide anakota nakukala na zaka zambili, banamuvinikila nama blageti , koma eve sanamvele kufunda. \v 2 Ba nchito bake banakamba kuli eve, "Tisakilile bwana watu mfumu musikana mungono wamene saziba mwamuna. Amutumikile mfumu na kumusamalila eve. Agone mumanja mwake kuti bwana watu mfumu akale ofunda."

1
01/03.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\v 3 Ndipo beve bana sakila musikana okongola mukati mwa malile yonse ya Israeli. Beve banapeza Abishagi mu Shunammiti naku mupeleka kwa mfumu. \v 4 Musikana uyu anali okongola kwambili. Anatumikila mfumu nakumusamalila, koma mfumu sanamuzibe.

1
01/05.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\v 5 Pa ntawi ija, Adoniya mwana wa Hagiti anazikweza, anati, "Nizankala mfumu". Ndipo eve anakonzekela magaleta na apakavalo pamozi na amuna 50 kuti batamangile pasogolo pake. \v 6 Batate bake sibanamuvute, anati, "Ni Chifukwa chani wachita ivi kapena ivo?" Ndipo Adoniya anali muntu okongola maningi, obadwa pambuyo pa Absalomu.

1
01/07.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\v 7 Anakambilana na Joabu mwana wa Zeruya na wansembe Abiyatara. Ndipo bana mukonka Adoniya nakumutandiza eve. \v 8 Koma wansembe Zadoki, Benaya mwana wa Yehoyada, Nathani muneneli, Simeyi, Rei, na bamuna bampamvu ba Davide sanamukonke Adoniya.

1
01/09.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\v 9 Adoniya anapeleka nsembe ya nkosa, na ngombe, ngombe yamafuta pafupi na mwala wa Zoheleti, pafupi na Eni Rogeli. Anaitana abale bake bonse, bana bamuna ba mfumu, na bamuna bonse ba ku Yuda, banchito ba mfumu. \v 10 Koma sanayitane Nathani muneneli, Benaya, bamuna bampamvu, kapena Solomoni mubale wake.

1
01/11.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\v 11 Pameneapo Nathani anakamba na Bathsheba mai wa Solomoni, kukamba , Kodi simunamvele kuti Adoniya mwana wa Haggithi ankala mfumu, ndipo Davide bwana watu saziba? \v 12 Manje leka nikupase nzelu, kuti uzipulumuse weka na moyo wa mwana wako Solomoni.

1
01/13.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\v 13 Yendani kuli Mfumu Davide; mukambe naye, ' Bwana wanga mfumu, kodi simunalumbile kuli mutumiki wanu, na kuti, '' Zoona Solomoni mwana wako azankala mfumu pambuyo panga, naku nkala pa mupando wanga wachifumu? Nanga bwanji Adoniya akulamulila? '' \v 14 Pamene ukali kukamba na mfumu, ine nizabwela pambuyo pako ndipo nizasimikizila mau yako. ”

1
01/15.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\v 15 Ndipo Bathsheba anangena muchipinda cha mfumu. Mfumu anali okalamba kwambili, ndipo Abishagi mu Shunammiti ankatumikila mfumu. \v 16 Bathsheba anapepeza na kupasa ulemu ku mfumu. Pameneapo mfumu anakamba kuti, "Mufuna chani?" \v 17 Anakamba kuli eve, Bwana wanga, munalumbila kuli mutumiki wanu na Yehova Mulungu wanu, kuti, 'Zoona Solomoni mwana wako azankala mfumu pambuyo panga, azankala pa mupando wanga wachifumu.

1
01/18.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\v 18 Manje, onani, Adoniya ndiye mfumu, koma imwe bwana wanga mfumu simuziba. \v 19 Wapeleka nsembe za ngombe zambili, na ngombe zoyina, na nkhosa, ndipo ayitana bana bonse bamuna ba mfumu, wansembe Abiyatara, na Joabi mukulu wa ankhondo, koma sanayitane Solomoni mutumiki wanu.

1
01/20.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\v 20 Pali imwe, bwana mfumu yanga , Aisraeli bonse ayangana pali imwe, kuti mubauuze wamene azankhala pamupando wanu wachifumu, bwana wanga. \v 21 Chamene chizachitika , pamene bwana mfumu yanga akasamila zanja na makolo ake, ine na mwana wanga Solomoni tizankhala ngati bakawalala. ”

1
01/22.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\v 22 Pamene eve anali kukamba na mfumu , muneneli Nathani anabwela. \v 23 Ndipo anchito anauuza mfumu, "Muneneli Nathani afika." Pamene eve anabwela pamanso pa mfumu, anawelama pamanso pa mfumu na nkhope yake pansi.

1
01/24.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\v 24 Nathani anakamba kuti, ''Bwana wanga mfumu, kodi munakamba kuti, 'Adoniya azankhala mfumu pambuyo panga, nakuankhala pa mupando wanga wacifumu?' \v 25 Popeza lelo ayenda kupeleka nsembe ng'ombe zambili, zonenepa, na nkhosa. ndipo ayitana bana bamuna bonse ba mfumu, kazembe wa nkhondo, na Abyatara wansembe. Ba kudya na kumwa pasogolo pake, nakukamba kuti, 'Mfumu Adoniya ankhale na umoyo wautali !'

1
01/26.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\v 26 Koma ine , wanchito wanu, wansembe Zadoki, Benaya mwana wa Yehoyada, na Solomoni wanchito wanu, sanatiyitaneko ife. \v 27 Kodi bwana mfumu yanga mwachita izi kosatiuuza , banchito banu, kuti nidani wamene azankhala pa mupando wachifumu pambuyo pake?''

1
01/28.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\v 28 Pameneapo Mfumu Davide anayankha nati, "Niyitanilenikoni Bathsheba kuti abwele kuli ine." Eve anabwela pamanso pa mfumu ndipo anayimilila pamanso pa mfumu. \v 29 Mfumu analumbila kuti, “Pali Yehova wamoyo, amene andiwombola ku mavuto yanga yonse, \v 30 monga ninalumbila kuli imwe na Yehova, Mulungu wa Israeli, kuti, 'Solomoni mwana wako azankhala mfumu pambuyo panga, ndipo azankhala pamupando wanga wachifumu mumalo mwanga, 'Nizachita izi lelo. " \v 31 Bathsheba anawelama mpaka nkhope yake pansi ndipo analemekeza mfumu nakukamba kuti, "Bwana wanga Mfumu Davide ankhale na umoyo osatha!"

1
01/32.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\v 32 Mfumu Davide anati, "Niyitanilenikoni Zadoki wansembe, Nathani mneneli, na Benaya mwana wa Yehoyada." Beve banabwela kuli mfumu. \v 33 Pameneapo mfumu nakamba kuti: “Tengani akapolo wa bwana wanu, ndipo mukwezeke mwana wanga Solomoni pa bulu yanga naku mupeleka ku Gihoni. \v 34 Lekani Zadoki wansembe na Nathani mneneli amuzoze ankhale mfumu ya Israeli nakuliza mapenga nakukamba kuti, Mfumu Solomoni ankhale na umoyo wautali!

1
01/35.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\v 35 Mwaichi muzabwela pambuyo pake, ndipo azabwela na nkunkhala pamupando wanga wachifumu. Namusankha kuti asogolele mfumu mumalo mwanga. Namusankha kuti ankhale musogoleli wa Israeli na Yuda. \v 36 ”Benaya mwana wa Yehoyada anayankha mfumu kuti, '' Chinkhale sochabe ! Lekani Yehova, Mulungu wa bwana mfumu yanga asimikizile izi. \v 37 Monga Yehova ankhala na bwana mfumu yanga, chinkhale sochabe kuli Solomoni, nakupanga mupando wake wachifumu koposa wa bwana wanga Mfumu Davide. ”

1
01/38.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\v 38 Pameneapo wansembe Zadoki, mneneli Nathani, Benaya mwana wa Yehoyada, na Kerethitesi na Pelethitesi banayenda naku kwezeka Solomoni pa bulu ya Mfumu Davide; banamutenga ku Gihoni. \v 39 Zadoki wansembe anatenga nyanga ya mafuta muchihema naku muzoza Solomoni. Pameneapo banaliza lipenga ndipo banthu bonse bana kamba kuti, “Mfumu Solomoni ankhale na umoyo wautali !” \v 40 Pameneapo banthu bonse banakwela patangu pake, ndipo banthu banaimba matolilo, na kukondwela na chisangalalo chachikulu; ndipo ziko inagwedezeka na phokoso zawo.

1
01/41.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\v 41 Adoniya na balendo bonse bamene banali naye banamvela pamene banasiliza kudya. Pamene Joabu anamvela kulila kwa lipenga anati, "Chifukwa nichani mu mzinda muli pokoso?" \v 42 Pamene anali kukamba , kunafika Jonathani mwana wa wansembe Abiyatara. Adoniya anati, genani, pakuti ndiwe munthu oyenela bwelesani uthenga wabwino.''

1
01/43.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\v 43 Pameneapo Jonathani anayankha Adoniya kuti, “Bwana wathu Mfumu Davide wayika Solomoni kunkhala mfumu, \v 44 ndipo atumiza wansembe Zadoki, Nathani muneneli, Benaya mwana wa Yehoyada, ma Kerethitesi na Pelethitesi. Bana yenza Solomoni pa bulu yama mfumu Davide. \v 45 Zadoki wansembe na Nathani mneneli anamuzoza kuti ankhale mfumu ku Gihoni, ndipo abwela kwameneuko alikusangalala, pakuti mu muzinda wonse wasanduka phokoso. Ndiye phokoso yamene mwamvela.

1
01/46.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\v 46 Koma, Solomoni ankhala pamupando wachifumu. \v 47 Ndiponso, banchito ba mfumu anabwela kudalisa bwana wathu Mfumu Davide, nakukamba kuti, Mulungu wanu apange zina ya Solomoni yopambana kuchila zina yanu , nakupanga mupando wake wacifumu upose mupando wanu wacifumu. \v 48 Ndipo mfumu inagwada pansi pa bedi. Mfumu anakamba kuti, 'Alemekezeke Yehova, Mulungu wa Israyeli, wamene apasa lelo munthu wonkhala pamupando wanga wachifumu pasiku yalelo , na manso yanga yaona ichi.'

1
01/49.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\v 49 Pamenepo balendo bonse ba Adoniya anachita mantha. Banayimilila ndipo aliyense anapita njila yake. \v 50 Adoniya anayopa Solomoni, nakunyamuka, nakugwila nyanga za guwa ya nsembe. \v 51 Kenako anauza Solomoni kuti: “Adoniya ayopa Mfumu Solomoni, chifukwa wagwila nyanga za guwa yansembe, nati, 'Mfumu Solomoni anilumbilile kuti sazapaya mtumiki wake na lupanga.''

1
01/52.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\v 52 Solomoni anakamba kuti, "Akazionesa ngati munthu oyenela, ngankhale sisi yake sizagwa pansi, koma ngati zoyipa zipezeka mwa eve, azafa." \v 53 Pameneapo mfumu Solomoni anatuma banthu, bamene anabwelesa Adoniya pa guwa ya nsembe. Anabwela nakugwadila Mfumu Solomoni, ndipo Solomoni anakamba kuti, "Yenda kunyumba kwako."

1
08/01.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\c 8 \v 1 Pamenepo Solomo anasonkanisa bakulu ba Israyeli, na bonse basogoleli ba mitundu, na basogoleli ba mabanja ya bana ba Israyeli, pamenso pake ku Yerusalemu, kuti akabwelese likasa ya chipangano cha Yehova kuchokela ku Mizinda ya Davide, ndiyo , Ziyoni. \v 2 Bamuna bonse ba Israeli banasonkana kwa Mfumu Solomoni ku madyelelo, mumwezi wa Etanimu, wamene ni mwezi wachisanu namba seveni.

1
08/03.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\v 3 Bakuluakulu bonse ba Israeli anabwela, na bansembe bananyamula likasa. \v 4 Bananyamula likasa la Yehova, mutenti yokumanilamo, na vopangiwa vonse vopatulika vamene vinali mutenti. Bansembe na Balevi banabwelesa izi. \v 5 Mfumu Solomoni na bosonkana bonse ba Israeli banasonkana pasogolo pa Likasa, kupeleka nkosa na ng'ombe zamene sibanakwanise kuzipenda.

1
08/06.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\v 6 Bansembe banangenesa likasa la chipangano cha Yehova kumalo yake, ku chipinda chamukati cha munyumba, Malo yoyela yopambana, pansi pa mapipiko ya Akerubi. \v 7 Chifukwa Akerubi banatambasula mapipiko yawo kumalo kwa Likasa, na kuvininkila Likasa na mitengo yake yonyamulila. \v 8 Mitengo inali itali kwambili chakuti kosilizila kwake yanali kuonekela kuchokela kumalo yoyela kusogolo kwa chipinda chamukati, koma siyanali kuonekela panja. yalipo mpaka lelo.

1
08/09.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\v 9 Munalibe kantu mulikasa koma chabe minyala ibibli yamene Mose anaikamo ku Horebe, pamene Yehova anapanga chipangano na bana ba Israyeli, pamene banachoka muziko ya Aigupto. \v 10 Panali kuti pamene bansembe banachoka mu malo yopatulika, kumbi inazula mu tempele ya Yehova. \v 11 Bansembe sibanakwanise kuimilila chifukwa cha kumbi, chifukwa ulemelelo wa Yehova unazula mu nyumba yake.

1
08/12.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\v 12 Pamenepo Solomoni anati, "Yehova akamba kuti azankala mumdima otikama, \v 13 koma nakumangila malo, malo yako yonkalamo muyayaya."

1
08/14.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\v 14 Ndipo mfumu inapindamuka na kudalisa bonse mupingo wa Isiraeli, pamene mupingo bonse wa Isiraeli unali woimilila. \v 15 Anakamba kuti, Alemekezeke Yehova Mulungu wa Israyeli, wamene anakamba na Davide tate wanga, na kukwanilisa na manja yake, kuti, \v 16 Kuyambila siku yamene ninachosa bantu banga Israyeli mu Aigupto, sininasanke muzinda kuchoka mumitundu yonse ya Israeli kuti amange nyumba, kuti zina yanga linkale pamenepo. Mwaichi, ninasankha Davide kuti alamulile banthu banga ba Israeli. '

1
08/17.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\v 17 Manje chinali mumutima wa Davide tate wanga ndi mtima womangira nyumba dzina la Yehova Mulungu wa Israyeli. \v 18 Koma Yehova anati kwa atate wanga Davide, Popeza munali mumutima mwanu kuti mumange nyumba pa zina yanga, munachita bwino kuli ichi mumitima mwanu. \v 19 Koma iwe suizamanga nyumba; Mumalo mwake, mwana wako wamwamuna, wamene azakabadwa mumusana mwako, azakamanga nyumba pa zina yanga. '

1
08/20.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\v 20 Yehova wakwanilisa mawu yamene anakamba, chifukwa nanyamuka mumalo mwa Davide batate banga, ndipo ninkala pamupando wachifumu wa Israyeli, monga Yehova anakamba. \v 21 Namanga nyumba mu zina ya Yehova, Mulungu wa Israyeli. Napanga malo ya likasa kwamene kuja, mwamene muli chipangano cha Yehova, chamene anapangana na makolo bathu pobachosa muziko ya Aigupto.

1
08/22.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\v 22 Solomoni anaimilila pasogolo pa guwa ya bansembe ya Yehova, pamenso pa banthu bonse ba Israyeli, natambasulira manja ake kumwamba. \v 23 Iye anati, "Yehova, Mulungu wa Israeli, palibe Mulungu wina monga imwe kumwamba kapena pansi pano wamene amasunga chipangano chake na bakapolo banu bamene bamayenda pamenso panu na mutima wabo bonse; \v 24 Imwe bamene mwasunga pamozi na mutumiki wanu Davide batate banga, vamene munamulonjeza. Zoona, munakamba na kamwa kanu ndipo mwakanilisa na kwanja kwanu, monga chili lelo.

2
08/25.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1,2 @@
\v 25 Manje, Yehova Mulungu wa Israyeli, chitani zamene munalonjeza mutumiki wanu Davide tate wanga, pamene munakamba kuti, Siuzasoba kunkala na muntu pamenso panga wakunkala pa mupando wachifumu wa Israyeli, ngati chabe bana
bako basamala mu kuyenda pasogolo panga, monga wayendela pasogolo panga.' \v 26 Manje, Mulungu wa Israyeli, lekani mau yanu yasimikizike, yamene mwayakamba kuli Davide mutumiki wanu tate wanga.

1
08/27.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\v 27 Ushe Mulungu nizoona azankala paziko lapansi? Onani, thambo yonse na kumwamba sikungankhale kukukwanisani imwe-nanga kuli bwanji kwa iyi tempele yamene namanga! \v 28 Ndipo lemekezani pempelo ya mutumiki wanu na kufuna kwake mozichepesa, Yehova Mulungu wanga; nvelani kulila na pempelo yamene mutumiki wanu apempela pamenso panu lelo.

1
08/29.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\v 29 Lekani Menso yanu yankhale yoseguka pali iyi tempele usiku na mu kukachisi uyu usiku na muzuba, kumalo yamene mwane kuti, Zina langa na kunkhalapo kwanga kuzankhala kwamene kuja, kuti mumvele mapemphelo yamene mutumiki wanu azapemphela pali yano malo. \v 30 Sopano mvelani pempelo y yozichepesa ya mutumiki wanu na banthu banu ba Israeli pamene tikupemphelela pamalo yano. Zoona, mvelani kuchokela kumalo kwamene munkala, kuchoka ku mwamba, ndipo mukanvela, kululukilani.

2
08/31.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1,2 @@
\v 31 Munthu akachimwila munzake wapafupi na akufunika
kulapila chipangano, ndipo ngati abwela na kulapila chipangano pasogolo pa guwa yanu yansembe munyumba ino, \v 32 mvelani kuchokela kumwamba na kuchita kantu. Weluzani bakapolo banu, kuweluza wosalungama na kuleta zamene achita pamutu wake. Muzikamba babwino kuti wosalakwa na kumupasa monga mu kuyela kwake.

1
08/33.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\v 33 Pamene banthu bako ba Israeli bagonjesedwa kuli badani chifukwa bakuchimwilani imwe, ngati batenukila kuli imwe, kukambilila pa zina yanu, nakupempela, nakufuna ubwino wanu mu tempele ino- \v 34 napapata nvelani kuchoka mumwamba na kukulukilila uchimo wa banthu banu ba Israeli; babweleseni futi kumalo yamene munapasa makolo yawo.

1
08/35.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\v 35 Pamene thambo yavalika ndipo kulibe mvula chifukwa banthu bakuchimwilani — ngati bapemphela bakalangana pamalo yano, kukamilila pa zina yanu, na kuchoka ku machimo yawo pamene mwabavutisa- \v 36 pamenepo mvelani kumwamba na kukululukila chimo ya mutumiki wanu na banthu banu ba Israeli, pamene mwabapunzisa njila yanu yabwino yamene bafunika kuyendamo. Tumani nvula pamalo yanu, yamene mwapasa kuli banthu banu monga cholowa chawo.

1
08/37.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\v 37 Tiyelekeze kuti muziko mwanu muli njala, kapena ngati muli matenda, chimphepo kapena kachilombo, zombe kapena malasankhuli; kapena kuti ngati mudani aukila zipata za muzi muziko yao, kapena kuti pali mulili uli wonse kapena matenda; \v 38 ndipo nichani ngati mapemphelo na zopempha zichokela kwa munthu, kapena na banthu banu bonse ba Israyeli, ali bonse aziba mulili wamene uyo mumutima mwake; atambasula manja yake kuyangana ku tempele iyi.

1
08/39.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\v 39 Ndipo mvelani kuchokela kumwamba, kumalo kwamene munkala, khululukilani na kuchitapo kanthu, ndipo bwezelani munthu aliyense pali vonse vamene achita; muzina mutima wake, chifukwa imwe ndipo imwe chabe muziba mitima ya bonse banthu. \v 40 Chitani izi kuti bakuyopeni masiku yonse yamene bazankhala mu malo yamene munapasa makolo yawo.

1
08/41.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\v 41 Komanso mulendo wonkhala pakati pa banthu banu ba Israeli: bakabwela kuchokela ku ziko yakutali chifukwa cha zina lanu, \v 42 chifukwa bazamvela za zina yanu yaikulu, na zanja yanu yamphamvu, na mukono wanu wokwezedwa, pamene babwela na kupemphela kuyangana ku tempele iy, \v 43 napapata mvelani kuchokela kumwamba, kumalo kwamene munkala, na kuchita chilichonse chamene mulendo akupempani imwe. Chitani ichi kuti banthu bonse paziko lapansi bazibe zina yanu na kukuopani, monga mwamene mumachitila banthu banu ba Israeli. Chitani ichi kuti bazibe kuti nyumba iyi yamene namanga iyitaniwa pa zina yanu.

1
08/44.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\v 44 Tiyelekeze kuti anthu anu apita kukamenyana na mudani, kudzera njira iliyonse yomwe mungatumize, ndipo akuganiza kuti akupemphera kwa inu, Yehova, kumzinda umene mwasankha, komanso kunyumba imene ndamangira dzina lanu. \v 45 Kenako mverani kumwambako pemphero lawo ndi pempho lawo, ndipo athandizeni pa zomwe akuchita.

1
08/46.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\v 46 Tiyelekeze kuti bakukuchimwilani, popeza palibe wamene samachimwa, ndipo muganiza kuti mwabakwiyila nakubapeleka mumanja mwa badani, kotelo kuti mudani wamene uyo azabatenga ukapolo kuziko yawo, ngakhale kutali kapena pafupi. \v 47 Ndiye ganizilani kuti bakumbukila kuti bali muziko yamene banatengewa ukapolo, nakuganiza kuti balapila nakupempha chifundo kwa imwe kuchokela kuziko ya bamene banabatenga. Tiyelekeze kuti banakamba, 'Tachita zolakwa ndipo tachimwa. Tachita vinthu voipa. '

1
08/48.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\v 48 Tiyelekeze kuti abwelela kwa inu na mitima yabo bonse na moyo wabo bonse mu ziko ya badani bawo bamene banabapoka, ndipo ngati bapemphela kwa imwe kusata ziko yawo, yamene munapasa makolo yawo, na muzinda wamene munausankha , na kunyumba yamene ndamangamo zina yanu.

1
08/49.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\v 49 Pamenepo kuchokera kumwamba, kwamene imwe munkala, mvelani imwe pemphero yabo na chopempa chabo kupempa tandizo, ndipo muzabalungamisa. \v 50 Mukululukire banthu banu bamene banakuchimwirani, na volakwa vawo vonse vamene banakulakwirani, ndipo mubachitire chifundo pamenso pa bamene bawagwira, na kubachitira chifundo bamene banabagwira.

1
08/51.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\v 51 Iwo ni banthu banu bamene munabasankha, bamene munawapulumutsa ku Iguputo ngati kuti mukuwotcha chitsulo. \v 52 Maso anu yakhale otsegukila pempho la ine mtumiki wanu, na zopempha za banthu banu Israyeli, kuti muwamvere iwo, pamene iwo alira kwa inu. \v 53 Pakuti munawapatula pakati pa anthu a mitundu yonse ya paziko lapansi yankhale banu, na kulandila malonjezano anu, monga umo munalongosolela na Mose mtumiki wanu, m'mene munaturutsa makolo athu m'Aigupto, Ambuye Yehova.

1
08/54.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\v 54 Ndipo kunali pamene anasiliza Solomoni kupemphela pemphelo ili lonse ndi kupemphera kwa Yehova, anauka pasogolo pa guwa la nsembe la Yehova, atagwada pansi, ndi manja ake atatambasulira kumwamba. \v 55 Iye anayimirira ndi kudalitsa mpingo wonse wa Israeli mofuwula, \v 56 nati, "Alemekezeke Yehova, amene wapatsa anthu ake Aisraeli mpumulo mwa kusunga malonjezo ake bonse. Palibe mawu amodzi omwe sanakwaniritsidwe pa malonjezo onse yabwino ya Yehova na Mose mutumiki wake.

1
08/57.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\v 57 Lekani Yehova Mulungu wathu ankhale naife monga anachitila na makolo bathu. \v 58 Asatisiye kapena kutitaya, kuti atembenukile mitima yathu kwa iye, kuti tikonke njila zake zonse, na kusunga malamulo yake, na malemba yake, yamene analamulila makolo yathu.

1
08/59.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\v 59 Vomelezani mawu aya nakamba, yamene napempha pamenso pa Yehova, yankale pafupi na Yehova Mulungu wathu usana na usiku, kuti atandize pa nchito ya mutumiki wake na mulandu wa anthu ake Israyeli, monga zifunikila siku na siku; \v 60 kuti anthu onse ya ziko lapansi bazibe kuti Yehova ndiye Mulungu, ndipo palibenso Mulungu wina; \v 61 Potero mutima wanu ukhale wokhulupirika kwa Yehova Mulungu wathu, kuyenda mumalemba ace, ndi kusunga malamulo ake, monga lero. "

1
08/62.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\v 62 Mwaichi mfumu na bonse Israeli bonse pamozi naye anapeleka nsembe kwa Yehova. \v 63 Solomo anapereka nsembe yoyamika kwa Yehova: ng'ombe zikwi makumi awili mphambu zibilii, na nkhosa 120,000. Momwemo mfumu na bana bonse ba Israyeli banapatula nyumba ya Yehova.

1
08/64.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\v 64 Pa siku yamene iyo mfumu inapatula pakati pa bwalo pasogolo pa tempele ya Yehova; pakuti pamenepo anapeleka nsembe zopseleza, na nsembe za mbeu, na mafuta ya nsembe zoyamika; zing'onozing'ono kulandila nsembe yopseleza, nsembe yambewu, ndi mafuta a nsembe zoyamika.

1
08/65.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\v 65 Pamenepo Solomoni anachita madyelelo pantawi yamene iyo, naba Israyeli bonse nayeve, musonkano waukulu, kuyambila ku Lebano Hamati kufikila ku musinje wa Aigupto, pamenso pa Yehova Mulungu wathu masiku yali seveni na yenangu masiku yali seveni, pamozi nimasiku yali fotini. \v 66 Pa siku lachisanu na chitatu anabatuma bantu kuti bapite, ndipo beve banadalisa mfumuyo na kupita kwawo na chimwemwe na mitima yokondwa chifukwa cha zabwino zonse zimene Yehova anachitira Davide mutumiki wake, na Israeli, bantu bake.

View File

@ -1 +0,0 @@
Mutu 13

1
20/01.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\c 20 \v 1 Beni-Hadadi mfumu ya Aramu anaunjika bankondo bake bonse pamozi. Panali naye mafumu yangono yangono yali 32, na makavalo na magareta. Anayenda pamwamba,kuzunguluka samaliya na kumenyana nayo \v 2 . Anatuma ntumi mu muzinda kuli Ahabu mfumu ya Israeli, nakukamba kuli eve, "Ben Hadadi akamba ivi: \v 3 'Siliva yako na golide yako ni yanga. Kuikilapo futi bakazi bako na bana, babwino maningi, manje ni banga. '"

1
20/04.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\v 4 Mfumu ya Israeli inayanka nakukamba ati, "Chili Monga mwamene wakambila, mbuye wanga mfumu. Ine na vonse vamene nilinavo ni vako." \v 5 ntumi zinabwela futi na kukamba ati, "Ben Hadadi akamba ivi, 'Ninakutumizila mau wokamba kuti unipase siliva yako, golide yako, bakazi bako, na bana bako. \v 6 Koma nizatuma bantchito banga kuli iwe mailo ntau yamene iyi, ndipo bazasakila sakila munyumba yako na mumanyumba yabanchito bako. Bazagwila na manja yao, nakuchosapo vonse vamene visangalasa menso yako.""

1
20/07.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\v 7 Pamene apo mfumu ya Israeli inayitana bakulu bonse ba muziko ija nakukamba ati, "Napapata zibani na kuwona mwamene muntu uyu afunila mavuto. Atumiza utenga kuli ine kuti atenge bakazi banga, bana, siliva na golide, ndipo ine sininamu kanile. " \v 8 Bakulu bonse na bantu bonse bana kamba kuli Ahabu "Musamumvele kapena kuchita vamene afuna."

1
20/09.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\v 9 Pamenepo Ahabu anauza bautenga ba Beni-hadadi kuti, "Uzani mbuye wanga mfumu kuti, 'Nivomeleza pavonse kuti munatumiza kapolo wanu kuchita paulendo woyamba, koma sinizavomela futi .'” ndipo ntumi zinachoka nakupeleka yanko kuli Ben Hadadi. \v 10 Ndipo Ben Hadadi anatumiza yanko yake kuli Ahabu, nakukamba ati, "Milungu zinichite so chabe nakuchilapo, " ngati milota ya mu samalia ingakwanile bantu bonse bamene banikonka kutengako che mukwanja,"

1
20/11.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\v 11 Mfumu ya Israeli inayanka nakukamba ati, "Uza Beni-Hadadi kuti, 'Palibe wamene avala zida zake ayenela kuzimvela monga azaivula.'” \v 12 Ben Hadadi anamvela utenga uwu pamene anali kumwa, eve na mfumu zinali pansi pake zamene zinali mumahema zawo. Ben Hadadi analamula banchito bake kuti, "Konzekelani nkondo." pamene apo banakonzekela mumalo ya nkondo kuti bamenyane na muzinda na muzinda.

1
20/13.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\v 13 Ndipo onani, muneneli anabwela kuli Ahabu mfumu ya Israyeli, nakukamba ati, Yehova akamba, ' wayiona gulu yankondo ikulu iyi? Ona, nizayiika mumanja mwako lelo, ndipo uzaziba kuti ndine Yehova. , \v 14 "Ahabu anayanka kuti, pali ndani?" Yehova anayanka nakukamba ati, "Pali banyamata bosebenzela bakazembe bamalo." Ndipo Ahabu anakamba ati, "Nindani wamene azayamba kumenya nkondo iyi?" Ndipo Yehova anayanka, "Iwe." \v 15 pamene apo Ahabu anasonkanisa banyamata bamene banalli kusebenzela bakazembe ba mumalo. Banali 232. Kuchoka apo anasonkanisa basilikali bonse, gulu yonse yankondo ya Isiraeli; yokwanila 7000.

1
20/16.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\v 16 Banayenda mu zuba. Ben Hadadi enze kumwa moba mutenti yake mpaka kukolewelatu, eve pamozi na mafumu yangonoyangono 32 yamene yenze kumutandiza. \v 17 Bankondo bafana bamene benzo tumikila bakazembe ba mumalo banayenda pasogolo. Ndipo Ben Hadadi anauziwa na bazondi bamene enze anatuma , "Bamuna bachokela ku Samariya."

1
20/18.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\v 18 Ben Hadadi anakamba, "Kaya ngati babwelela mutendele olo nkondo nkondo, baleteni bamoyo." \v 19 Mwaicho banyamata benzo tumikila bakazembe ba madela banayenda kuchoka mu muzinda ndipo gulu yabankondo inabakonka.

1
20/20.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\v 20 Aliyense anapaya muzake. Baku Aaramu banataba ndipo Isiraeli anaba konka pambuyo. Beni-Hadadi mfumu yaku Aramu anataba pakavalo pamozi na bamuna boyendesa makavalo. \v 21 kuchoka apo mfumu ya Isiraeli inayenda kumenya makavalo na magaleta yao, na kupaya baku Aramu bambili maningi.

1
20/22.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\v 22 Manje muneneli anabwela kuli mfumu ya Isilayeli nakukamba kuli yeve," Yenda, ukazilimbise, na kumvesesa na kukonza vameme uchita, chifukwa pakusila kwa chaka mfumu ya Aramu izabwela kumenyana naiwe futi. \v 23 Banchito ba mfumu ya Aramu banakamba kuli eve, "Mulungu wabo ni Mulungu wa mapili. Ndiye chifukwa chake benze nampamvu kuchila ise. Koma manje tiyeni timenyane nabo muchigwa, ndipo tizankala bolimba kubachila.

1
20/24.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\v 24 Mwaicho muchite ivi: Chosani mamfumu yonse pamalo yao yaulamulilo wao nakufakapo bakulu bakulu bankondo. \v 25 Nyamulani gulu yankondo monga yamene munataya — kavalo mumalo mwa kavalo na galeta mumalo ya galeta- kuti tingamenyane nabo muchigwa. Pamene apo mosakaikila tizankala na mpamvu kubachila . Mwaicho Ben Hadadi anamvela vamene banamuuza na kuchita vamene banamulangiza.

1
20/26.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\v 26 Pambuyo poyamba chaka chamanje, Ben Hadadi anasonkanisa ma Aaramu na kuyenda ku Afeki kumenyana na Isirayeli. \v 27 Bantu baku isilayeli banasonkanisiwa na kupasiwa kuti bamenyane nabo. Bantu baku isilayeli banamanga misasa pasogolo pabo monga tumagulu tubili twa mbuzi, koma ma Aaramu banazula malo yonse.

1
20/28.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\v 28 Pamene apo muntu wa Mulungu anabwela pafupi na kukamba na mfumu ya Isirayeli ati, " Yehova akamba: 'Chifukwa ba Aaramu bakamba kuti Yehova ndiye mulungu wa kumapili, koma si Mulungu wa vigwa, nizaika iyi gulu yambili ya nkondo mukwanja yako ndipo uzaziba kuti ndine Yehova.""

1
20/29.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\v 29 Mwaicho magulu yankondo yanasonkana moyanganana pa masiku 7. Manje pasiku yasabata nkondo inayamba. Bantu baku isilayeli banapaya basilikali baku Aaramu 100,000 pasiku imozi. \v 30 Banasala banatabila ku Afeki, mumuzinda, ndipo chipupa chinagwela pali bamuna 27,000 bamene banasala. Ben Hadadi anataba nakuyenda mu muzinda, muchipinda chamukati.

1
20/31.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\v 31 Bancito ba Ben Hadadi banakamba kuli eve, "Ona manje, tamvela kuti mfumu za nyumba ya Isirayeli ni mfumu zachifundo.Napapata tiyeni timange vovala vamasaka muchiuno mwatu na ntambo kumitu zatu, na kuyenda kuli mfumu yaku Isirayeli.Mwamwai azapulumusa umoyo wako. " \v 32 Mwaicho banavala vovala vamasaka muchiuno na ntambo mumitu zao na kuyenda kuli mfumu ya Isirayeli nakukamba ati, "wanchito wanu Ben Hadadi anakamba, 'Napapata lekani ninkale wa moyo.'” Ahabu anakamba, "akali wa moyo? ni mubale wanga. "

1
20/33.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\v 33 Manje bamuna banali kumvelela chizindikilo chilichonse chochokela kuli Ahabu, pameneapo mwamusanga banamuyanka kuti, "Ehe, mubale wako Ben Hadadi ali moyo." Mwaicho Ahabu anakamba , " yenda ukamulete." \v 34 Ndipo Ben-Hadadi anakamba kuli Ahabu, , "Nikubwezelani mizinda zamene batate banga banapoka batate banu, ndipo mungazipangile pogulisila mu Damasiko, mwamene batate banga banachitila ku Samariya." Ahabu anayanka, "Nizakuleka uyende na pangano iyi." ndipo Ahabu anachita naeve pangano, nakumuleka ayende.

1
20/35.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\v 35 Muntu winango, umozi pali bana ba baneneli, anakamba kuli munzake kupitila mu mau ya Yehova, "Napapata nimenye." Koma mwamuna anakana kumumenya. \v 36 Mwaicho muneneli anakamba kuli muneneli munzake, "Chifukwa sunamvele mawu ya Yehova, pamene apo ukanisiya, nkalamu izakupaya." Pamene apo mwamuna anayenda, nkalamu inabwela pali eve na kumupaya.

1
20/37.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\v 37 Kuchoka apo muneneli anapeza muntu winango nakukamba, "Napapata nimenye." ndipo mwamuna uyo anamumenya na kumupanga chilonda. \v 38 Ndipo muneneli anayenda nakuyembekeza mfumu panjila; anali anazibis na nsalu pamenso yake.

1
20/39.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\v 39 Pamene mfumu inapitilapo, muneneli analila kuli mfumu nakukamba ati, "Wantchito wako anayenda mukutenta kwa nkondo, ndipo musilikali winanangu ana imilila nakuleta muntu kuli ine na kukamba, 'onani muntu uyu. Ngati mu njila iliyonse asoba, moyo wako uzapasiwa mumalo mwa moyo wake, olo uzafunika kulipila ndalama imozi ya siliva. ' \v 40 Koma chifukwa wanchito wako enze kungo yenda yenda uku na uku, muntu anataba. " ndipo mfumu ya Israeli inamuwuza kuti, "Ichi ndiye chizankala chilango chako- iwe mwine wake wasanka."

1
20/41.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\v 41 Pamene apo muneneli mwamusanga musanga anachosa chomangilila mumenso mwake, ndipo mfumu ya Israeli inazindikila kuti eve enze umozi wa baneneli. \v 42 Ndipo muneneli anakamba kuli mfumu, Yehova akamba, "Pakuti walekelela muntu wamene nenze nina peleka kuchionongeko, moyo wako uzankala mumalo mwa moyo wake, na bantu mumalo mwa bantu bake. \v 43 mwaicho Mfumu ya Israeli inayenda kunyumba kwake yokolewa na namkwiyo, nakufika ku Samaliya.

View File

@ -34,33 +34,13 @@
"parent_draft": {},
"translators": [
"Timothy Muzgatama",
"Mzamose Mtonga"
"Mzamose Mtonga",
"MWAKA NAMUCHIMBA MWANZA",
"BRIAN SIMWAKA"
],
"finished_chunks": [
"front-title",
"01-title",
"01-01",
"01-03",
"01-05",
"01-07",
"01-09",
"01-11",
"01-13",
"01-15",
"01-18",
"01-20",
"01-22",
"01-24",
"01-26",
"01-28",
"01-32",
"01-35",
"01-38",
"01-41",
"01-43",
"01-46",
"01-49",
"01-52",
"02-title",
"02-01",
"02-05",
@ -163,35 +143,6 @@
"07-50",
"07-51",
"08-title",
"08-01",
"08-03",
"08-06",
"08-09",
"08-12",
"08-14",
"08-17",
"08-20",
"08-22",
"08-25",
"08-27",
"08-29",
"08-31",
"08-33",
"08-35",
"08-37",
"08-39",
"08-41",
"08-44",
"08-46",
"08-48",
"08-49",
"08-51",
"08-54",
"08-57",
"08-59",
"08-62",
"08-64",
"08-65",
"09-title",
"09-01",
"09-03",
@ -259,18 +210,6 @@
"12-31",
"12-33",
"13-title",
"13-01",
"13-04",
"13-06",
"13-08",
"13-14",
"13-18",
"13-20",
"13-23",
"13-26",
"13-29",
"13-31",
"13-33",
"14-title",
"14-01",
"14-04",
@ -361,26 +300,6 @@
"19-19",
"19-21",
"20-title",
"20-01",
"20-04",
"20-07",
"20-09",
"20-11",
"20-13",
"20-16",
"20-18",
"20-20",
"20-22",
"20-24",
"20-26",
"20-28",
"20-29",
"20-31",
"20-33",
"20-35",
"20-37",
"20-39",
"20-41",
"21-title",
"21-01",
"21-03",