Thu Apr 18 2024 15:41:07 GMT+0200 (South Africa Standard Time)
This commit is contained in:
parent
92053883bc
commit
aa1a9671f6
|
@ -1 +1 @@
|
|||
\v 5 \v 6 Pakuti Solomo anatsatira Asitoreti mulungu wamkazi wa Asidoni, ndi kutsatira Moleki fano lonyansa la Aamoni. Solomoni anachita choipa pamaso pa Yehova; sanatsata Yehova ndi mtima wonse monga anachitira Davide atate wake.
|
||||
\v 5 Pakuti Solomo anatsatira Asitoreti mulungu wamkazi wa Asidoni, ndi kutsatira Moleki fano lonyansa la Aamoni. \v 6 Solomoni anachita choipa pamaso pa Yehova; sanatsata Yehova ndi mtima wonse monga anachitira Davide atate wake.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 7 Pamenepo Solomoni anamangira Kemosi fano lonyansa la Mowabu malo okwezeka paphiri la kum'mawa kwa Yerusalemu, ndiponso anamangira Moleki fano lonyansa la ana a Amoni. \v 8 Anamangiranso akazi ake onse achilendo malo okwezeka, amene ankafukizapo nsembe zautsi ndi kupereka nsembe kwa milungu yawo.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 9 Yehova anakwiyira Solomo chifukwa mtima wake unapatuka kwa iye, Mulungu wa Isiraeli, ngakhale kuti anaonekera kwa iye kawiri, \v 10 ndipo anamulamula kuti asatsatire milungu ina. Koma Solomo sanamvere zimene Yehova anamuuza.
|
|
@ -228,6 +228,7 @@
|
|||
"11-title",
|
||||
"11-01",
|
||||
"11-03",
|
||||
"11-05",
|
||||
"11-07",
|
||||
"11-09",
|
||||
"11-11",
|
||||
|
|
Loading…
Reference in New Issue