Thu Oct 07 2021 20:37:45 GMT+0200 (Central Africa Time)
This commit is contained in:
parent
4b9026d2f4
commit
a05320a5c2
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 3 Solomo anayankha mafunso ake onse. Palibe chomwe adafunsa chomwe amfumu sanayankhe. \v 4 Mfumukazi ya ku Seba itaona nzeru zonse za Solomoni, nyumba yachifumu yomwe anamanga, \v 5 chakudya patebulo lake, malo okhala antchito ake, ntchito za antchito ake ndi zovala zawo, omuperekera chikho, ndi momwe amaperekera nsembe zopereka m'nyumba ya Yehova, munalibe mpweya mwa iye.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 6 Iye anati kwa mfumu, "Zowonadi, zomwe ndinamva m mydziko langa la mawu anu ndi nzeru zanu. \v 7 Sindinakhulupirire zomwe ndinamva mpaka nditabwera kuno, ndipo tsopano maso anga aona. Wandiwuza za nzeru zako ndi chuma chako, Wachita zoposa mbiri zimene ndinamva.
|
|
@ -0,0 +1 @@
|
|||
\v 8 Odala akazi anu, ndi odala atumiki anu amene amayimirira pamaso panu nthawi zonse, chifukwa amva nzeru zanu. \v 9 Alemekezeke Yehova Mulungu wanu, amene anakondwera nanu, amene anakuikani pampando wachifumu wa Israyeli. Popeza Yehova anakonda Israyeli kosatha, anakuyikani kuti mukhale mfumu, kuti muweruze ndi kuchita chilungamo.
|
|
@ -207,6 +207,10 @@
|
|||
"09-24",
|
||||
"09-25",
|
||||
"09-26",
|
||||
"10-title"
|
||||
"10-title",
|
||||
"10-01",
|
||||
"10-03",
|
||||
"10-06",
|
||||
"10-08"
|
||||
]
|
||||
}
|
Loading…
Reference in New Issue