Fri Oct 08 2021 10:58:16 GMT+0200 (Central Africa Time)

This commit is contained in:
Timothy Muzgatama 2021-10-08 10:58:17 +02:00
parent 09a090527d
commit 9b4e76e8c5
4 changed files with 6 additions and 1 deletions

1
22/13.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\v 13 Mthenga amene anapita kukaitana Mikaya analankhula naye, nati, "Taona tsopano, mawu a aneneri alengeza zabwino kwa mfumu ndi mawu amodzi. Chonde lolani mawu anu akhale ngati mmodzi wa iwo ndikunena zabwino." \v 14 Mikaya anayankha kuti, "Pali Yehova wamoyo, ndidzanena ndi Yehova." \v 15 Atafika kwa mfumu, mfumu inamufunsa kuti, "Mikaya, kodi tipite ku Ramoti Giliyadi kunkhondo, kapena ayi?" Mikaya anayankha kuti, "Pita ukapambane. Yehova apereka m'manja mwa mfumu."

1
22/16.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\v 16 Ndipo mfumu inanena naye, Ndikufunira kangati kuti ulumbire kuti usandiuze kanthu koma chowonadi m'dzina la Yehova? \v 17 Pamenepo Mikaya anati, "Ndinaona Aisraeli onse atamwazikana kumapiri, ngati nkhosa zopanda m'busa, ndipo Yehova anati, 'Amenewa alibe m'busa. Aliyense abwerere ku nyumba yake mwamtendere."

1
22/18.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\v 18 Ndipo mfumu ya Israyeli inati kwa Yehosafati, Kodi sindinakuuza kuti adzanenera zabwino za ine, koma zoipa zokhazokha? \v 19 Pamenepo Mikaya anati, "Chifukwa chake imvani mawu a Yehova: Ine ndinawona Yehova atakhala pa mpando wake wachifumu, ndipo makamu onse akumwamba anaimirira pambali pake kudzanja lamanja ndi lamanzere. \v 20 atha kukwera kukagwera ku Ramoti Gileadi? ' Mmodzi wa iwo ananena izi ndipo wina ananena zakutizakuti.

View File

@ -399,6 +399,8 @@
"22-03",
"22-05",
"22-07",
"22-10"
"22-10",
"22-13",
"22-16"
]
}