diff --git a/10/28.txt b/10/28.txt index 1e54065..0324148 100644 --- a/10/28.txt +++ b/10/28.txt @@ -1 +1 @@ -\v 28 \v 29 Akavalo amene anali a Solomo anagula ku Iguputo, + ndipo Kuwe ndi amalonda a mfumu anali kuwagula ku Kuwe. Magareta anakwera kucokera ku Aigupto pa mtengo wa masekeli mazana asanu ndi limodzi a siliva, ndi akavalo masekeli 150. Ambiri a iwo anagulitsidwa kwa mafumu onse a Ahiti ndi Aaramu. \ No newline at end of file +\v 28 Akavalo amene anali a Solomo anagula ku Iguputo, + ndipo Kuwe ndi amalonda a mfumu anali kuwagula ku Kuwe. \v 29 Magareta anakwera kucokera ku Aigupto pa mtengo wa masekeli mazana asanu ndi limodzi a siliva, ndi akavalo masekeli 150. Ambiri a iwo anagulitsidwa kwa mafumu onse a Ahiti ndi Aaramu. \ No newline at end of file diff --git a/11/01.txt b/11/01.txt new file mode 100644 index 0000000..48d57d9 --- /dev/null +++ b/11/01.txt @@ -0,0 +1 @@ +\c 11 \v 1 Tsopano Mfumu Solomo inakonda akazi ambiri achilendo, kuphatikizapo mwana wamkazi wa Farao, akazi achimowabu, Aamoni, Aedomu, Asidoni, ndi Ahiti. \v 2 Anali a mitundu imene Yehova anauza ana a Isiraeli kuti: “Musapite pakati pawo kukakwatira kapena kukwatiwa, kapena kuti iwowo asalowe pakati panu, chifukwa adzatembenuzira mitima yanu kwa milungu yawo. Mosasamala kanthu za lamulo limeneli, Solomo anakonda akazi ameneŵa mwachikondi. \ No newline at end of file diff --git a/11/03.txt b/11/03.txt new file mode 100644 index 0000000..95349e9 --- /dev/null +++ b/11/03.txt @@ -0,0 +1 @@ +\v 3 Solomoni anali ndi akazi mazana asanu ndi awiri, ana aakazi, ndi adzakazi mazana atatu. Akazi ake anapatutsa mtima wake. \v 4 Pakuti pamene Solomo anakalamba, akazi ake anapambutsa mtima wake atsate milungu yina; mtima wake sunadzipereka kwathunthu kwa Yehova Mulungu wake, monga mtima wa Davide atate wake. \ No newline at end of file diff --git a/11/05.txt b/11/05.txt new file mode 100644 index 0000000..9d2523c --- /dev/null +++ b/11/05.txt @@ -0,0 +1 @@ +\v 5 \v 6 Pakuti Solomo anatsatira Asitoreti mulungu wamkazi wa Asidoni, ndi kutsatira Moleki fano lonyansa la Aamoni. Solomoni anachita choipa pamaso pa Yehova; sanatsata Yehova ndi mtima wonse monga anachitira Davide atate wake. \ No newline at end of file diff --git a/11/title.txt b/11/title.txt new file mode 100644 index 0000000..cb80763 --- /dev/null +++ b/11/title.txt @@ -0,0 +1 @@ +Mutu 11 \ No newline at end of file diff --git a/manifest.json b/manifest.json index 7373b0a..9186749 100644 --- a/manifest.json +++ b/manifest.json @@ -224,10 +224,10 @@ "10-21", "10-23", "10-26", + "10-28", "11-title", "11-01", "11-03", - "11-05", "11-07", "11-09", "11-11",