Sat Apr 20 2024 09:39:08 GMT+0200 (South Africa Standard Time)

This commit is contained in:
Timothy Muzgatama 2024-04-20 09:39:09 +02:00
parent 14a333bc0f
commit 4103de871f
5 changed files with 4 additions and 1 deletions

1
21/19.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\v 19 Ukamuuze kuti Yehova akuti, 'Kodi wapha ndi kulanda? Pamenepo udzamuuza kuti Yehova akuti, Pamalo pamene agalu ananyambita magazi a Naboti, agalu adzanyambita magazi ako, inde magazi ako.’” \v 20 Ahabu anauza Eliya kuti: “Kodi wandipeza mdani wanga? Eliya anayankha kuti: “Ndakupeza, chifukwa wadzigulitsa kuti uchite zoipa pamaso pa Yehova.

1
21/21.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\v 21 Yehova atero kwa iwe, Taona, ndidzakutengera tsoka, ndi kutha ndi kupha Ahabu ana aamuna onse, ndi kapolo, ndi mfulu mIsrayeli; \v 22 Ndidzayesa banja lako ngati banja la Yerobiamu mwana wa Nebati, ndi banja la Basa mwana wa Ahiya, popeza wandikwiyitsa ine, ndi kucimwitsa Israyeli.

1
21/23.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\v 23 Yehova ananenanso za Yezebeli, kuti, Agalu adzadya Yezebeli pafupi ndi linga la Yezreeli. \v 24 Aliyense wa Ahabu akafera mumzinda, agalu adzamudya. ndipo mbalame za mumlengalenga zidzadya aliyense wakufa kuthengo.

1
22/05.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\v 5 Yehosafati anauza mfumu ya Isiraeli kuti: “Chonde funsani malangizo kwa Yehova kuti muyambe kuchita chiyani. \v 6 Pamenepo mfumu ya Israyeli inasonkhanitsa aneneri mazana anai, nanena nao, Ndipite kunkhondo ku Ramoti Giliyadi, kapena ndisapite? Iwo anati, "Umbani, pakuti Yehova adzaupereka m'manja mwa mfumu."

View File

@ -400,7 +400,6 @@
"22-title",
"22-01",
"22-03",
"22-05",
"22-07",
"22-10",
"22-13",