Thu Apr 18 2024 15:23:05 GMT+0200 (South Africa Standard Time)

This commit is contained in:
Timothy Muzgatama 2024-04-18 15:23:06 +02:00
parent ac6388268a
commit 109ca23e16
3 changed files with 3 additions and 0 deletions

1
09/10.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\v 10 Ndipo kunali, pakutha zaka makumi awiri, Solomo anatsiriza kumanga nyumba ziwirizo, Kacisi wa Yehova ndi nyumba ya mfumu. \v 11 Tsopano Hiramu mfumu ya Turo anapatsa Solomo mitengo ya mkungudza ndi mikungudza, ndi golidi, zonse zimene Solomo anafuna, motero Mfumu Solomo inapatsa Hiramu mizinda 20 mdziko la Galileya.

1
09/12.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\v 12 Hiramu anaturuka ku Turo kukaona midzi imene Solomo anampatsa, koma sanamkomera. \v 13 Ndipo Hiramu anati, Ndi midzi yotani iyi wandipatsa ine, mbale wanga? Hiramu anawatcha Dziko la Kabul, limene amalitchulabe mpaka pano. \v 14 Hiramu anatumiza kwa mfumu matalente 120 agolide.

1
09/15.txt Normal file
View File

@ -0,0 +1 @@
\v 15 Izi ndi nkhani za anthu okakamiza amene Mfumu Solomo analamula kuti amange kachisi wa Yehova ndi nyumba yake yachifumu, Milo, linga la Yerusalemu, Hazori, Megido, ndi Gezeri. \v 16 Farao mfumu ya Aigupto anakwera nalanda Gezeri. Anautentha ndi kupha Akanani a mumzindawo. Kenako Farao anapereka mzindawu kwa mwana wake wamkazi, mkazi wa Solomo, monga mphatso ya ukwati.