nya-x-nyanja_1ki_text_reg/21/27.txt

1 line
436 B
Plaintext
Raw Permalink Normal View History

\v 27 Ahabu atamva mawu amenewa, anangamba zovala zake nkuvala chiguduli nkusala kudya, nkugona chiguduli ndi kumva chisoni kwambiri. \v 28 Pamenepo mawu a Yehova anafika kwa Eliya wa ku Tisibe, kuti: \v 29 “Kodi waona mmene Ahabu wadzichepetsera pamaso panga? Popeza wadzichepetsa pamaso panga, sindidzabweretsa tsoka limene likubwera mmasiku ake, + chifukwa mtsiku la mwana wake ndidzabweretsa tsoka pa banja lake.